1Atonthozeni, atonthozeni anthu anga,
2Ayankhuleni moleza mtima anthu a ku Yerusalemu
3Mawu a wofuwula mʼchipululu akuti,
4Chigwa chilichonse achidzaze.
5Ndipo ulemerero wa Yehova udzaonekera,
6Wina ananena kuti, “Lengeza.”
7Udzu umanyala ndipo maluwa amafota
8Udzu umanyala ndipo maluwa amafota,
9Iwe amene ukulengeza nkhani yabwino ku Ziyoni,
10Taonani, Ambuye Yehova akubwera mwamphamvu,
11Iye adzasamalira nkhosa zake ngati mʼbusa:
12Kodi ndani akhoza kuyeza kuchuluka kwa madzi a mʼnyanja ndi chikhatho chake,
13Ndani anapereka malangizo kwa Mzimu wa Yehova
14Kodi Yehova anapemphapo nzeru kwa yani kuti akhale wopenya,
15Ndithudi mitundu ya anthu ili ngati dontho la madzi ochoka mu mtsuko.
16Nkhalango ya ku Lebanoni singakwanire nkhuni zosonkhera moto pa guwa lansembe,
17Pamaso pa Yehova mitundu yonse ya anthu ili ngati chinthu chopandapake;
18Kodi tsono Mulungu mungamuyerekeze ndi yani?
19Likakhala fano, mʼmisiri ndiye analipanga
20Mʼmphawi amene sangathe kupeza ngakhale chopereka nsembe chotere
21Kodi simukudziwa?
22Yehova amene amakhala pa mpando wake waufumu kumwamba ndiye analenga dziko lapansi,
23Amatsitsa pansi mafumu amphamvu
24Inde, iwo ali ngati mbewu zimene zangodzalidwa kumene
25Woyera uja akuti, “Kodi mudzandiyerekeza Ine ndi yani?
26Tayangʼanani mlengalenga ndipo onani.
27Iwe Yakobo, chifukwa chiyani umanena
28Kodi simukudziwa?
29Iye amalimbitsa ofowoka
30Ngakhale achinyamata amalefuka ndi kufowoka,
31koma iwo amene amakhulupirira Yehova