1Uthenga wonena za chipululu cha mʼmbali mwa Nyanja.
2Ine ndaona zinthu zoopsa mʼmasomphenya:
3Chifukwa cha zimenezi thupi langa likunjenjemera ndi mantha,
4Mtima wanga ukugunda,
5Ankhondo a ku Elamu ndi Mediya akukonza matebulo,
6Zimene Ambuye akunena kwa ine ndi izi;
7Taonani, anthu akubwera ali pa akavalo
8Ndipo mlondayo anafuwula kuti,
9Taonani, uyo munthu akubwera atakwera pa galeta
10Inu anthu anga opunthidwa ndi kupetedwa ngati tirigu,
11Uthenga wonena za Duma:
12Mlonda akuyankha kuti,
13Uthenga wonena za Arabiya:
14perekani madzi kwa anthu aludzu.
15Iwo akuthawa malupanga,
16Zimene Ambuye akunena kwa ine ndi izi: “Chaka chimodzi chisanathe, potsata mmene amawerengera munthu waganyu, ulemerero wonse wa Kedara udzatheratu.
17Mwa anthu okoka uta, ankhondo a ku Kedara opulumuka adzakhala owerengeka.” Wayankhula ndi Yehova Mulungu wa Israeli.