We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 11

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 10 Yesaya Yesaya 12 →

1Padzatuluka mphukira pa tsinde la Yese

2Mzimu wa Yehova udzakhala pa iye

3Ndipo kuopa Yehova ndiye chidzakhale chinthu chomukondweretsa.

4koma amphawi adzawaweruza mwachilungamo,

5Chilungamo chidzakhala ngati lamba wake

6Mʼmbulu udzakhala pamodzi ndi mwana wankhosa,

7Ngʼombe yayikazi ndi chimbalangondo zidzadya pamodzi,

8Mwana wakhanda adzasewera pa dzenje la mamba,

9Sipadzakhala chilichonse chopweteka kapena chowononga

10Tsiku limenelo mfumu yatsopano yochokera pa Muzu wa Yese idzakhala ngati chizindikiro kwa anthu a mitundu yonse. Mitundu ya anthu idzasonkhana kwa Iye, ndipo malo awo okhalapo adzakhala aulemerero.

11Tsiku limenelo Ambuye adzatambasula dzanja lake kachiwiri kuti awombole anthu ake otsalira ku Asiriya, ku Igupto, ku Patirosi, Kusi, ku Elamu, ku Sinana, ku Hamati ndi pa zilumba za nyanja yamchere.

12Adzakwezera mitundu ya anthu mbendera,

13Nsanje ya Efereimu idzatha,

14Yuda ndi Efereimu adzathira nkhondo pa Afilisti mbali ya kumadzulo;

15Yehova adzaphwetsa

16Padzakhala msewu waukulu woti ayendepo anthu ake otsalira

← Yesaya 10 Yesaya Yesaya 12 →