1Padzatuluka mphukira pa tsinde la Yese
2Mzimu wa Yehova udzakhala pa iye
3Ndipo kuopa Yehova ndiye chidzakhale chinthu chomukondweretsa.
4koma amphawi adzawaweruza mwachilungamo,
5Chilungamo chidzakhala ngati lamba wake
6Mʼmbulu udzakhala pamodzi ndi mwana wankhosa,
7Ngʼombe yayikazi ndi chimbalangondo zidzadya pamodzi,
8Mwana wakhanda adzasewera pa dzenje la mamba,
9Sipadzakhala chilichonse chopweteka kapena chowononga
10Tsiku limenelo mfumu yatsopano yochokera pa Muzu wa Yese idzakhala ngati chizindikiro kwa anthu a mitundu yonse. Mitundu ya anthu idzasonkhana kwa Iye, ndipo malo awo okhalapo adzakhala aulemerero.
11Tsiku limenelo Ambuye adzatambasula dzanja lake kachiwiri kuti awombole anthu ake otsalira ku Asiriya, ku Igupto, ku Patirosi, Kusi, ku Elamu, ku Sinana, ku Hamati ndi pa zilumba za nyanja yamchere.
12Adzakwezera mitundu ya anthu mbendera,
13Nsanje ya Efereimu idzatha,
14Yuda ndi Efereimu adzathira nkhondo pa Afilisti mbali ya kumadzulo;
15Yehova adzaphwetsa
16Padzakhala msewu waukulu woti ayendepo anthu ake otsalira