We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Deuteronomo 33

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Deuteronomo 32 Deuteronomo Deuteronomo 34 →

1Awa ndi madalitso amene Mose, munthu wa Mulungu, anawapereka kwa Aisraeli asanafe.

2Iye anati:

3Ndithu ndinu amene mumakonda anthu anu;

4malamulo amene Mose anatipatsa,

5Iye anali mfumu ya Yesuruni

6“Lolani Rubeni akhale ndi moyo ndipo asafe,

7Ndipo ponena za Yuda anati:

8Za fuko la Alevi anati:

9Iye ananena za abambo ake ndi amayi ake kuti,

10Iye amaphunzitsa Yakobo malangizo anu

11Inu Yehova, dalitsani luso lake lonse

12Za fuko la Benjamini anati:

13Za fuko la Yosefe anati:

14ndi zinthu zambiri zimene zimacha ndi dzuwa

15ndi zipatso zabwino kwambiri zochokera mʼmapiri amakedzanawa

16ndi mphatso zabwino kwambiri zochokera pa dziko lapansi ndi zonse zimene zili mʼmenemo

17Ulemerero wake uli ngati ngʼombe yayimuna yoyamba kubadwa;

18Za fuko la Zebuloni anati:

19Adzayitanira mitundu ya anthu kumapiri,

20Za fuko la Gadi anati:

21Iye anadzisankhira dziko labwino kwambiri;

22Za fuko la Dani anati:

23Za fuko la Nafutali anati:

24Za fuko la Aseri anati:

25Zotsekera za zipata zako zidzakhala za chitsulo ndi za mkuwa,

26“Palibe wina wofanana ndi Mulungu wa Yesuruni,

27Mulungu wamuyaya ndiye pothawirapo pathu,

28Motero Israeli adzakhala yekha mwamtendere;

29Iwe Israeli, ndiwe wodala!

← Deuteronomo 32 Deuteronomo Deuteronomo 34 →