1Ukanakhala kuti ndiwe mlongo wanga,
2Ndikanakutenga
3Mutu wanga watsamira dzanja lake lamanzere
4Inu akazi a ku Yerusalemu, ndithu ndikukupemphani:
5Kodi ndani uyo akutuluka ku chipululuyo,
6Undiyike pamtima pako ngati chidindo,
7Madzi ochuluka sangachizimitse chikondi,
8Ife tili naye mlongo wathu wamngʼono,
9Ngati iye ndi khoma,
10Ine ndili ngati khoma,
11Solomoni anali ndi munda wampesa ku Baala-Hamoni;
12Koma munda wanga wampesa ndi wangawanga ndiponso wa ine ndekha.
13Iwe amene umakhala mʼminda
14Fulumira wokondedwa wanga,