We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Nyimbo ya Solomoni 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Nyimbo ya Solomoni 1 Nyimbo ya Solomoni Nyimbo ya Solomoni 3 →

1Ine ndine duwa la ku Saroni,

2Monga duwa lokongola pakati pa minga

3Monga mtengo wa apulosi pakati pa mitengo ya mʼnkhalango

4Iye wanditengera ku nyumba yaphwando,

5Undidyetse keke ya mphesa zowuma,

6Mutu wanga watsamira dzanja lake lamanzere,

7Inu akazi a ku Yerusalemu, ndithu ndikukupemphani

8Tamverani bwenzi langa!

9Bwenzi langa ali ngati gwape kapena mwana wa mbawala.

10Bwenzi langa anayankha ndipo anati kwa ine,

11Ona, nyengo yozizira yatha;

12Maluwa ayamba kuoneka pa dziko lapansi;

13Mtengo wankhuyu ukubereka zipatso zake zoyambirira;

14Nkhunda yanga yokhala mʼmingʼalu ya thanthwe,

15Mutigwirire nkhandwe,

16Bwenzi langa ndi wangadi ndipo ine ndine wake;

17Kamphepo kamadzulo kakayamba kuwuzira

← Nyimbo ya Solomoni 1 Nyimbo ya Solomoni Nyimbo ya Solomoni 3 →