1Ine ndine duwa la ku Saroni,
2Monga duwa lokongola pakati pa minga
3Monga mtengo wa apulosi pakati pa mitengo ya mʼnkhalango
4Iye wanditengera ku nyumba yaphwando,
5Undidyetse keke ya mphesa zowuma,
6Mutu wanga watsamira dzanja lake lamanzere,
7Inu akazi a ku Yerusalemu, ndithu ndikukupemphani
8Tamverani bwenzi langa!
9Bwenzi langa ali ngati gwape kapena mwana wa mbawala.
10Bwenzi langa anayankha ndipo anati kwa ine,
11Ona, nyengo yozizira yatha;
12Maluwa ayamba kuoneka pa dziko lapansi;
13Mtengo wankhuyu ukubereka zipatso zake zoyambirira;
14Nkhunda yanga yokhala mʼmingʼalu ya thanthwe,
15Mutigwirire nkhandwe,
16Bwenzi langa ndi wangadi ndipo ine ndine wake;
17Kamphepo kamadzulo kakayamba kuwuzira