We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Nyimbo ya Solomoni 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

Nyimbo ya Solomoni Nyimbo ya Solomoni 2 →

1Nyimbo ya Solomoni, nyimbo yoposa nyimbo zonse.

2Undipsompsone ndi milomo yako

3Mafuta ako odzola ndi onunkhira bwino;

4Nditenge ndipo ndizikutsata, tiye tifulumire!

5Ndine wakuda, komatu ndine wokongola,

6Musandiyangʼane monyoza chifukwa ndine wakuda,

7Ndiwuze iwe, amene ndimakukonda, kumene umadyetsa ziweto zako

8Ngati sukudziwa iwe wokongola kwambiri kuposa akazi ena,

9Iwe bwenzi langa,

10Masaya ako ndi okongola ndi ndolo zamʼmakutuzo,

11Tidzakupangira ndolo zagolide

12Pamene mfumu inali pa malo ake odyera,

13Wokondedwa wanga ali ngati kathumba ka mure kwa ine,

14Wokondedwa wanga ali ngati mpukutu wa maluwa ofiira,

15Iwe wokondedwa wanga, ndiwe wokongoladi!

16Iwe bwenzi langa, ndiwe wokongoladi!

17Mitanda ya nyumba yathu ndi ya mkungudza,

Nyimbo ya Solomoni Nyimbo ya Solomoni 2 →