1Ine ndinaona Ambuye atayima pambali pa guwa lansembe, ndipo anati:
2Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa,
3Ngakhale atakabisala pamwamba pa phiri la Karimeli,
4Ngakhale adani awo awakusire ku ukapolo,
5Ambuye Yehova Wamphamvuzonse
6Iye amene amamanga malo ake okhalamo kumwamba,
7“Kodi kwa Ine, inu Aisraeli, simuli
8“Taonani, maso a Ambuye Yehova
9“Pakuti ndidzalamula,
10Anthu onse ochimwa pakati pa anthu anga
11“Tsiku limenelo ndidzabwezeretsa
12kuti adzatengenso otsala a Edomu
13Yehova akunena kuti
14Ndidzawabwezeranso pabwino anthu anga Aisraeli;
15Ndidzakhazika Aisraeli mʼdziko mwawo,