We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Amosi 9

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Amosi 8 Amosi

1Ine ndinaona Ambuye atayima pambali pa guwa lansembe, ndipo anati:

2Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa,

3Ngakhale atakabisala pamwamba pa phiri la Karimeli,

4Ngakhale adani awo awakusire ku ukapolo,

5Ambuye Yehova Wamphamvuzonse

6Iye amene amamanga malo ake okhalamo kumwamba,

7“Kodi kwa Ine, inu Aisraeli, simuli

8“Taonani, maso a Ambuye Yehova

9“Pakuti ndidzalamula,

10Anthu onse ochimwa pakati pa anthu anga

11“Tsiku limenelo ndidzabwezeretsa

12kuti adzatengenso otsala a Edomu

13Yehova akunena kuti

14Ndidzawabwezeranso pabwino anthu anga Aisraeli;

15Ndidzakhazika Aisraeli mʼdziko mwawo,

← Amosi 8 Amosi