1Israeli, imva mawu awa, nyimbo ya maliro imene ndikuyimba za iweyo:
2“Namwali Israeli wagwa,
3Ambuye Yehova akuti,
4Zimene Yehova akunena kwa nyumba ya Israeli ndi izi:
5musafunefune Beteli,
6Funani Yehova kuti mukhale ndi moyo,
7Inu amene mumasandutsa chiweruzo cholungama kukhala chowawa
8(Iye amene analenga nyenyezi za Nsangwe ndi Akamwiniatsatana,
9Iyeyo amabweretsa chiwonongeko modzidzimutsa pa anthu amphamvu
10inu mumadana ndi amene amadzudzula mʼbwalo la milandu
11Mumapondereza munthu wosauka
12Pakuti Ine ndikudziwa kuchuluka kwa zolakwa zanu
13Nʼchifukwa chake pa nthawi yotere munthu wanzeru sayankhulapo kanthu,
14Muyike mtima wanu pa zabwino osati pa zoyipa,
15Mudane ndi zoyipa, mukonde zabwino;
16Choncho izi ndi zimene Ambuye, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, akunena:
17Mʼminda yonse ya mpesa mudzakhala kulira kokhakokha,
18Tsoka kwa inu amene mumalakalaka
19Lidzakhala ngati tsiku limene munthu pothawa mkango
20Kodi tsiku la Yehova silidzakhala mdima osati kuwala,
21“Ndimadana nawo masiku anu achikondwerero ndipo ndimawanyoza;
22Ngakhale mupereke nsembe zopsereza ndi nsembe zachakudya,
23Musandisokose nazo nyimbo zanu!
24Koma chiweruzo cholungama chiyende ngati madzi,
25“Kodi pa zaka makumi anayi zimene munakhala mʼchipululu muja
26Inu mwanyamula kachisi wa mfumu yanu,
27Nʼchifukwa chake Ine ndidzakupititsani ku ukapolo, kutali kupitirira ku Damasiko,”