We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

1 Mbiri 6

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← 1 Mbiri 5 1 Mbiri 1 Mbiri 7 →

1Ana a Levi anali awa:

2Ana a Kohati anali awa:

3Ana a Amramu anali awa:

4Eliezara anabereka Finehasi,

5Abisuwa anabereka Buki,

6Uzi anabereka Zerahiya,

7Merayoti anabereka Amariya,

8Ahitubi anabereka Zadoki,

9Ahimaazi anabereka Azariya,

10Yohanani anabereka Azariya (uyu ndi amene anatumikira monga wansembe mʼNyumba ya Mulungu imene Solomoni anamanga mu Yerusalemu),

11Azariya anabereka Amariya,

12Ahitubi anabereka Zadoki,

13Salumu anabereka Hilikiya,

14Azariya anabereka Seraya,

15Yehozadaki anagwidwa ukapolo pamene Yehova analola Nebukadinezara kuti agwire ukapolo Yuda ndi Yerusalemu.

16Ana a Levi anali awa:

17Mayina a ana a Geresomu ndi awa:

18Ana a Kohati anali awa:

19Ana a Merari anali awa:

20Ana a Geresomu ndi awa:

21Yowa,

22Zidzukulu za Kohati ndi izi:

23Elikana,

24Tahati, Urieli,

25Zidzukulu za Elikana ndi izi:

26Elikana, Zofai,

27Eliabu,

28Ana a Samueli ndi awa:

29Zidzukulu za Merari ndi izi:

30Simea, Hagiya

31Awa ndi anthu amene Davide anawayika kuti aziyangʼanira mayimbidwe mʼNyumba ya Yehova, Bokosi la Chipangano litabwera kudzakhala mʼmenemo.

32Iwo ankatumikira akuyimba nyimbo pa khomo la malo opatulika, tenti ya msonkhano, mpaka Solomoni atamanga Nyumba ya Yehova mu Yerusalemu. Iwo ankagwira ntchito zawo potsata malamulo amene anawapatsa.

33Mayina a anthuwo, pamodzi ndi ana awo, anali awa:

34mwana wa Elikana, mwana wa Yerohamu,

35mwana wa Zufi, mwana wa Elikana,

36mwana wa Elikana, mwana wa Yoweli,

37mwana wa Tahati, mwana wa Asiri,

38mwana wa Izihari, mwana wa Kohati,

39ndi Asafu mʼbale wake, amene ankatumikira ku dzanja lake lamanja:

40mwana wa Mikayeli, mwana wa Baaseya,

41mwana wa Etini,

42mwana wa Etani, mwana wa Zima,

43mwana wa Yahati,

44ndipo abale awo ena anali a banja la Merari amene amatumikira ku dzanja lake lamanzere:

45mwana wa Hasabiya,

46mwana wa Amizi, mwana wa Bani,

47mwana wa Mahili,

48Abale awo Alevi anapatsidwa ntchito zina zonse ku malo opatulika ku nyumba ya Mulungu.

49Koma Aaroni ndi zidzukulu zake anali amene amapereka nsembe pa guwa lansembe zopsereza ndi pa guwa lansembe zofukiza pamodzi ndi zonse zimene zimachitika ku malo opatulika kwambiri, kuchita mwambo wopepesera Israeli, potsata zonse zimene Mose mtumiki wa Mulungu anawalamulira.

50Ana a Aaroni ndi zidzukulu zake anali awa:

51Buki,

52Merayoti, Amariya,

53Zadoki

54Malo amene iwo anapatsidwa kuti likhale dziko lawo ndi awa: (Malowa anapatsidwa kwa zidzukulu za Aaroni zimene zinali za banja la Kohati, chifukwa malo oyamba kugawidwa anali awo).

55Iwo anapatsidwa Hebroni mʼdziko la Yuda ndi madera odyetsera ziweto ozungulira malowa.

56Koma minda ndi midzi yozungulira mzindawo zinapatsidwa kwa Kalebe mwana wa Yefune.

57Kotero zidzukulu za Aaroni zinapatsidwa Hebroni (mzinda wopulumukirako), ndi Libina, Yatiri, Esitemowa,

58Hileni, Debri,

59Asani, Yuta ndi Beti-Semesi pamodzi ndi madera odyetsera ziweto ozungulira malowa.

60Ndipo ku fuko la Benjamini anapatsidwa Gibiyoni, Geba, Alemeti ndi Anatoti, pamodzi ndi madera odyetsera ziweto ozungulira malowa.

61Zidzukulu zotsala za Kohati anazigawira midzi khumi kuchokera ku mabanja a fuko la theka la Manase.

62Zidzukulu za Geresomu banja ndi banja zinapatsidwa mizinda 13 kuchokera ku mafuko a Isakara, Aseri ndi Nafutali, ndi gawo lina la fuko la Manase limene lili ku Basani.

63Zidzukulu za Merari banja ndi banja zinapatsidwa mizinda khumi ndi iwiri kuchokera ku mafuko a Rubeni, Gadi ndi Zebuloni.

64Kotero Aisraeli anapatsa Alevi mizindayi ndi madera a msipu ozungulira malowa.

65Kuchokera ku mafuko a Yuda, Simeoni ndi Benjamini anawapatsa mizinda imene inawatchula kale mayina.

66Mabanja ena a Kohati anapatsidwanso malo kuchokera ku fuko la Efereimu.

67Kuchokera ku dziko lamapiri la Efereimu anapatsidwa Sekemu (mzinda wopulumukirako) ndi Gezeri,

68Yokineamu, Beti-Horoni,

69Ayaloni ndi Gati-Rimoni, pamodzi ndi madera odyetsera ziweto ozungulira.

70Ndipo kuchokera ku theka la fuko la Manase, Aisraeli anapereka Aneri ndi Bileamu pamodzi ndi madera odyetsera ziweto kwa mabanja ena onse a Kohati.

71Ageresomu analandira malo awa:

72Kuchokera ku fuko la Isakara

73Ramoti ndi Anemu, pamodzi ndi malo ake odyetsera ziweto;

74kuchokera ku fuko la Aseri

75Hukoki ndi Rehobu, pamodzi ndi malo ake odyetsera ziweto;

76ndipo kuchokera ku fuko la Nafutali

77Amerari (Alevi ena onse) analandira madera awa:

78Kuchokera ku fuko la Rubeni kutsidya kwa Yorodani, kummawa kwa Yeriko,

79Kedemoti ndi Mefaati, pamodzi ndi malo ake odyetsera ziweto;

80ndipo kuchokera ku fuko la Gadi

81Hesiboni ndi Yazeri, pamodzi ndi malo ake odyetsera ziweto.

← 1 Mbiri 5 1 Mbiri 1 Mbiri 7 →