We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

1 Mbiri 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← 1 Mbiri 2 1 Mbiri 1 Mbiri 4 →

1Ana aamuna a Davide amene anabadwira ku Hebroni anali awa:

2wachitatu anali Abisalomu, mwana wa Maaka mwana wa Talimai mfumu ya Gesuri;

3wachisanu anali Sefatiya, amayi ake anali Abitali;

4Ana asanu ndi mmodzi awa a Davide anabadwira ku Hebroni kumene analamulirako zaka zisanu ndi ziwiri ndi miyezi isanu ndi umodzi.

5ndipo ana amene anabadwira ku Yerusalemuko anali awa:

6Anaberekanso Ibihari, Elisua, Elipeleti,

7Noga, Nefegi, Yafiya,

8Elisama, Eliada ndi Elifeleti, onse analipo asanu ndi anayi.

9Onsewa anali ana a Davide, osawerengera ana a azikazi. Ndipo mlongo wawo anali Tamara.

10Mwana wa Solomoni anali Rehabiamu,

11Yehosafati anabereka Yehoramu,

12Yowasi anabereka Amaziya,

13Yotamu anabereka Ahazi,

14Manase anabereka Amoni,

15Ana a Yosiya anali awa:

16Ana a Yehoyakimu:

17Zidzukulu za Yekoniya wa mʼndende zinali izi:

18Malikiramu, Pedaya, Senazara, Yekamiya, Hosama ndi Nedabiya.

19Ana a Pedaya anali awa:

20Panalinso ana ena asanu awa:

21Zidzukulu za Hananiya zinali izi:

22Zidzukulu za Sekaniya zinali izi:

23Ana a Neariya anali awa:

24Ana a Eliyoenai: Hodaviya, Eliyasibu, Pelaya, Akubu,

← 1 Mbiri 2 1 Mbiri 1 Mbiri 4 →