1Inu Yehova, kumbukirani Davide
2Iye analumbira kwa Yehova
3“Sindidzalowa mʼnyumba mwanga
4sindidzalola kuti maso anga agone,
5mpaka nditamupezera malo Yehova,
6Zoonadi, tinamva za Bokosi la Chipangano ku Efurata,
7“Tiyeni tipite ku malo ake okhalamo;
8‘Dzukani Yehova, ndipo bwerani ku malo anu opumulira,
9Ansembe anu avekedwe chilungamo;
10Chifukwa cha Davide mtumiki wanu,
11Yehova analumbira kwa Davide,
12ngati ana ako azisunga pangano langa
13Pakuti Yehova wasankha Ziyoni,
14“Awa ndi malo anga opumapo ku nthawi za nthawi;
15Ndidzadalitsa mzindawu ndi zinthu zambiri;
16Ndidzaveka ansembe ake chipulumutso,
17“Pano ndidzachulukitsa mphamvu za Davide
18Ndidzaveka adani ake manyazi,