We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 132

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 131 Masalimo Masalimo 133 →

1Inu Yehova, kumbukirani Davide

2Iye analumbira kwa Yehova

3“Sindidzalowa mʼnyumba mwanga

4sindidzalola kuti maso anga agone,

5mpaka nditamupezera malo Yehova,

6Zoonadi, tinamva za Bokosi la Chipangano ku Efurata,

7“Tiyeni tipite ku malo ake okhalamo;

8‘Dzukani Yehova, ndipo bwerani ku malo anu opumulira,

9Ansembe anu avekedwe chilungamo;

10Chifukwa cha Davide mtumiki wanu,

11Yehova analumbira kwa Davide,

12ngati ana ako azisunga pangano langa

13Pakuti Yehova wasankha Ziyoni,

14“Awa ndi malo anga opumapo ku nthawi za nthawi;

15Ndidzadalitsa mzindawu ndi zinthu zambiri;

16Ndidzaveka ansembe ake chipulumutso,

17“Pano ndidzachulukitsa mphamvu za Davide

18Ndidzaveka adani ake manyazi,

← Masalimo 131 Masalimo Masalimo 133 →