We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Hoseya 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Hoseya 1 Hoseya Hoseya 3 →

1“Nena kwa abale ako kuti, ‘Ndinu anthu anga,’ kwa alongo ako kuti ‘Ndinu okondedwa anga.’ ”

2“Dzudzulani amayi anu, adzudzuleni iwo,

3Akapanda kutero ndidzamuvula,

4Sindidzaonetsa chikondi changa pa ana ake,

5Amayi awo akhala akuchita zachiwerewere

6Choncho njira yake ndidzayitseka ndi minga;

7Adzathamangira zibwenzi zake koma sadzazipeza;

8Iye sanazindikire kuti ndine amene

9“Choncho Ine ndidzamulanda tirigu wanga pa nthawi yokolola,

10Motero tsopano ndidzaonetsa maliseche ake

11Ndidzathetsa zikondwerero zake zonse:

12Ndidzawononga mitengo yake ya mpesa ndi mitengo yake yamkuyu,

13Ndidzamulanga chifukwa cha masiku

14“Koma tsopano ndidzamukopa mkaziyo;

15Kumeneko ndidzamubwezera minda yake ya mpesa,

16“Tsiku limeneli,” Yehova akuti,

17Ndidzachotsa mayina a Abaala pakamwa pake;

18Tsiku limenelo ndidzachita pangano

19Ndidzakutomera kuti ukhale mkazi wanga mpaka muyaya;

20Ndidzakutomera mokhulupirika

21“Tsiku limenelo Ine ndidzayankha,”

22ndipo nthaka idzamvera kupempha kwa tirigu,

23Ndidzadzala Israeli mʼdziko kuti akhale wanga:

← Hoseya 1 Hoseya Hoseya 3 →