1“Nena kwa abale ako kuti, ‘Ndinu anthu anga,’ kwa alongo ako kuti ‘Ndinu okondedwa anga.’ ”
2“Dzudzulani amayi anu, adzudzuleni iwo,
3Akapanda kutero ndidzamuvula,
4Sindidzaonetsa chikondi changa pa ana ake,
5Amayi awo akhala akuchita zachiwerewere
6Choncho njira yake ndidzayitseka ndi minga;
7Adzathamangira zibwenzi zake koma sadzazipeza;
8Iye sanazindikire kuti ndine amene
9“Choncho Ine ndidzamulanda tirigu wanga pa nthawi yokolola,
10Motero tsopano ndidzaonetsa maliseche ake
11Ndidzathetsa zikondwerero zake zonse:
12Ndidzawononga mitengo yake ya mpesa ndi mitengo yake yamkuyu,
13Ndidzamulanga chifukwa cha masiku
14“Koma tsopano ndidzamukopa mkaziyo;
15Kumeneko ndidzamubwezera minda yake ya mpesa,
16“Tsiku limeneli,” Yehova akuti,
17Ndidzachotsa mayina a Abaala pakamwa pake;
18Tsiku limenelo ndidzachita pangano
19Ndidzakutomera kuti ukhale mkazi wanga mpaka muyaya;
20Ndidzakutomera mokhulupirika
21“Tsiku limenelo Ine ndidzayankha,”
22ndipo nthaka idzamvera kupempha kwa tirigu,
23Ndidzadzala Israeli mʼdziko kuti akhale wanga: