1Masomphenya a Obadiya.
2“Taona, ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina;
3Kudzikuza kwa mtima wako kwakusocheretsa,
4Koma ngakhale umawuluka ngati chiwombankhanga
5“Anthu akuba akanabwera kwa iwe,
6Koma Esau adzalandidwa zinthu zonse,
7Anthu onse ogwirizana nawo adzakupirikitsira kumalire;
8Yehova akunena kuti, “Tsiku limenelo,
9Ankhondo ako, iwe Temani, adzachita mantha,
10Chifukwa cha nkhanza zimene unachitira mʼbale wako Yakobo,
11Pamene adani
12Iwe sunayenera kunyoza mʼbale wako
13Iwe sunayenera kudutsa pa zipata za anthu anga
14Sunayenera kudikirira pamphambano ya misewu
15“Tsiku la Yehova layandikira
16Iwe unamwa pa phiri langa loyera,
17Koma pa Phiri la Ziyoni padzakhala chipulumutso;
18Nyumba ya Yakobo idzasanduka moto
19Anthu ochokera ku Negevi adzakhala
20Aisraeli amene ali ku ukapolo
21Opulumukawo adzapita ku Phiri la Ziyoni