We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Obadiya 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

Obadiya

1Masomphenya a Obadiya.

2“Taona, ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina;

3Kudzikuza kwa mtima wako kwakusocheretsa,

4Koma ngakhale umawuluka ngati chiwombankhanga

5“Anthu akuba akanabwera kwa iwe,

6Koma Esau adzalandidwa zinthu zonse,

7Anthu onse ogwirizana nawo adzakupirikitsira kumalire;

8Yehova akunena kuti, “Tsiku limenelo,

9Ankhondo ako, iwe Temani, adzachita mantha,

10Chifukwa cha nkhanza zimene unachitira mʼbale wako Yakobo,

11Pamene adani

12Iwe sunayenera kunyoza mʼbale wako

13Iwe sunayenera kudutsa pa zipata za anthu anga

14Sunayenera kudikirira pamphambano ya misewu

15“Tsiku la Yehova layandikira

16Iwe unamwa pa phiri langa loyera,

17Koma pa Phiri la Ziyoni padzakhala chipulumutso;

18Nyumba ya Yakobo idzasanduka moto

19Anthu ochokera ku Negevi adzakhala

20Aisraeli amene ali ku ukapolo

21Opulumukawo adzapita ku Phiri la Ziyoni

Obadiya