1Yehova anati kwa Yobu:
2“Kodi iwe ufuna kukangana ndi Wamphamvuzonse?
3Pamenepo Yobu anayankha Yehova:
4“Ine sindili kanthu konse,
5Ndinayankhula kamodzi, koma pano ndilibe yankho,
6Ndipo Yehova anayankha Yobu mʼkamvuluvulu kuti,
7“Tsopano vala dzilimbe ngati mwamuna;
8“Kodi iwe unganyoze chiweruzo changa cholungama?
9Kodi uli ndi dzanja monga la Mulungu,
10Ngati zili choncho udzikometsere ndi ulemerero ndi kukongola,
11Tsanula ukali wako wosefukirawo,
12Uyangʼane aliyense wodzikweza ndipo umutsitse,
13Onsewo uwakwirire pamodzi mfumbi;
14Ukatero Ine ndidzakuvomereza
15“Taganiza za mvuwu,
16Mphamvu zake ndi zazikulu kwambiri,
17Mchira wake umayima tolotolo ngati mtengo wamkungudza;
18Mafupa ake ali ngati mapayipi amkuwa,
19Mvuwuyo ndi yayikulu mwa zolengedwa za Mulungu,
20Imapeza chakudya chake ku mtunda
21Imagona pa tsinde pa zitsamba za mipeta,
22Imaphimbika ndi mthunzi wazitsamba za mipeta;
23Madzi a mu mtsinje akakokoma, sichita mantha,
24Kodi alipo amene angathe kukola mvuwu ndi mbedza