We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Oweruza 5

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Oweruza 4 Oweruza Oweruza 6 →

1“Tsiku limenelo Debora ndi Baraki mwana wa Abinoamu anayimba nyimbo iyi:

2“Popeza kuti atsogoleri anatsogoleradi mʼdziko la Israeli;

3“Imvani inu mafumu! Tcherani khutu, atsogoleri inu!

4“Inu Yehova, pamene munkatuluka mu Seiri,

5Mapiri anagwedezeka pamaso pa Yehova,

6“Pa nthawi ya Samugara mwana wa Anati,

7Anthu a ku midzi anathawa; mu Israeli munalibe midzi

8Pamene anasankha milungu ina,

9Mtima wanga uli ndi atsogoleri a Israeli,

10“Inu okwera pa abulu oyera,

11Ku zitsime, kutali ndi phokoso la a mauta;

12Anati, ‘Tsogolera ndiwe, Debora, tsogolera;

13“Kenaka anthu okhulupirika anatsatira atsogoleri awo;

14Anakalowa mʼchigwa kuchokera ku Efereimu;

15Olamulira a Isakara anali pamodzi ndi Debora;

16Chifukwa chiyani munangokhala ku makola a nkhosa nʼkumangomvetsera

17Agiliyadi anatsala pa tsidya la Yorodani.

18Azebuloni ndi anthu amene anayika moyo wawo mʼzoopsa.

19“Mafumu anabwera, anachita nkhondo;

20Ngakhalenso nyenyezi zakumwamba zinachita nkhondo,

21Mtsinje wa Kisoni unawakokolola,

22Ndipo ziboda za ngʼombe zazimuna zinachita phokoso lalikulu,

23Mngelo wa Yehova anati ‘Tembererani Merozi.’

24“Akhale wodala kupambana akazi onse,

25Munthu uja anapempha madzi akumwa, koma iye anamupatsa mkaka;

26Anatenga chikhomo cha tenti mʼdzanja lake,

27Anathifukira ku mapazi a mkaziyo nagwa,

28“Amayi ake a Sisera anasuzumira pa zenera;

29Amayi ake anzeru kwambiri anamuyankha,

30‘Kodi iwo sakufunafuna zofunkha kuti agawane;

31“Choncho Yehova! adani anu onse awonongeke,

← Oweruza 4 Oweruza Oweruza 6 →