We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yeremiya 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yeremiya 1 Yeremiya Yeremiya 3 →

1Yehova anandiwuza kuti,

2“Pita ukalengeze kwa anthu a ku Yerusalemu kuti Yehova akuti,

3Israeli anali wopatulika wa Yehova,

4Imvani mawu a Yehova, inu zidzukulu za Yakobo,

5Yehova akuti,

6Iwo sanafunse nʼkomwe kuti, ‘Kodi Yehova ali kuti,

7Ndinakufikitsani ku dziko lachonde

8Ansembe nawonso sanafunse kuti,

9“Chifukwa chake Ine ndidzakuyimbaninso mlandu,”

10Pitani kumadzulo ku chilumba cha Kitimu, ndipo mukaone,

11Kodi ulipo mtundu wa anthu uliwonse umene unasinthapo milungu yake?

12Inu mayiko akumwamba, dabwani ndi zimenezi,

13“Popeza anthu anga achita machimo awiri:

14Israeli si wantchito kapena kapolo wobadwira mʼnyumba, ayi.

15Adani ake abangulira

16Ndiponso Aigupto a ku Mefisi ndi a ku Tapanesi

17Zimenezitu zakuchitikirani

18Tsopano mudzapindula chiyani mukapita ku Igupto,

19Kuyipa kwanuko kudzakulangani;

20“Kuyambira kalekale inu munathyola goli lanu

21Ine ndinakudzala iwe ngati mtengo wampesa wosankhika;

22Ngakhale utasamba ndi soda

23“Iwe ukunena bwanji kuti, ‘Ine sindinadziyipitse;

24wakhala ngati mbidzi yozolowera mʼchipululu,

25Iwe usathamange, nsapato zingakuthere kuphazi

26“Monga momwe mbala imachitira manyazi pamene yagwidwa,

27Iwo amawuza mtengo kuti, ‘Iwe ndiwe abambo athu,’

28Nanga ili kuti milungu yanu imene munadzipangira nokha?

29“Kodi mukundizengeranji mlandu?

30“Ine ndinalanga anthu ako popanda phindu;

31“Inu anthu a mʼbado uno, ganizirani bwino mawu a Yehova:

32Kodi namwali amayiwala zokongoletsera zake,

33Mumadziwa bwino njira zopezera zibwenzi!

34Ngakhale pa zovala zako anthu amapezapo

35inu mukunena kuti, ‘Ndife osalakwa,

36Chifukwa chiyani

37Mudzachokanso kumeneko

← Yeremiya 1 Yeremiya Yeremiya 3 →