We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yona 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yona 1 Yona Yona 3 →

1Yona ali mʼmimba mwa chinsomba chija anapemphera kwa Yehova Mulungu wake.

2Iye anati:

3Munandiponya mʼnyanja yozama,

4Ndinati, ‘Ine ndachotsedwa

5Madzi wondimiza anandichititsa mantha,

6Ndinatsikira kunsi ndithu, mʼtsinde mwa mapiri;

7“Pamene moyo wanga umachoka mwa ine,

8“Iwo amene amagwiritsitsa mafano achabechabe

9Koma ine ndidzapereka kwa Inu nsembe

10Ndipo Yehova analamula chinsomba chija, ndipo chinakamusanza Yonayo mʼmbali mwa nyanja.

← Yona 1 Yona Yona 3 →