1Yona ali mʼmimba mwa chinsomba chija anapemphera kwa Yehova Mulungu wake.
2Iye anati:
3Munandiponya mʼnyanja yozama,
4Ndinati, ‘Ine ndachotsedwa
5Madzi wondimiza anandichititsa mantha,
6Ndinatsikira kunsi ndithu, mʼtsinde mwa mapiri;
7“Pamene moyo wanga umachoka mwa ine,
8“Iwo amene amagwiritsitsa mafano achabechabe
9Koma ine ndidzapereka kwa Inu nsembe
10Ndipo Yehova analamula chinsomba chija, ndipo chinakamusanza Yonayo mʼmbali mwa nyanja.