1Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2“Kodi mudzakhala mukundizunza mpaka liti,
3Inuyo mwandinyoza kwambiri;
4Ngati ndi zoona kuti ine ndasochera,
5Ngati ndithudi mukudziyika nokha pamwamba panga,
6pamenepa dziwani kuti Mulungu wandilakwira
7“Ngakhale ndifuwule kuti, ‘Akundizunza!’ Palibe wondiyankha;
8Mulungu wanditsekera njira yanga kotero sindingathe kudutsa;
9Iye wandilanda ulemu wanga
10Wandiphwanyaphwanya mbali zonse ndipo ndatheratu;
11Wandikwiyira ndipo
12Ankhondo ake akubwera kwa ine mwamphamvu,
13“Mulungu wandisiyanitsa ndi abale anga;
14Abale anga andithawa;
15Anthu odzacheza ku nyumba kwanga ndiponso antchito anga aakazi andisandutsa mlendo;
16Ndikayitana wa ntchito wanga, iye sandiyankha,
17Mpweya wanga umamunyansa mkazi wanga;
18Inde, ngakhale ana amandinyoza;
19Anzanga onse apamtima amanyansidwa nane;
20Ndangotsala khungu ndi mafupa okhaokha;
21“Mvereni chisoni, inu abwenzi anga, mvereni chisoni,
22Chifukwa chiyani mukundilondola ngati Mulungu?
23“Aa, achikhala mawu anga analembedwa,
24akanalembedwa pa mwala ndi chitsulo,
25Koma ndikudziwa kuti mpulumutsi wanga ali ndi moyo,
26Ndipo khungu langa litatha nʼkuwonongeka,
27Ine ndemwe ndidzamuona Iye
28“Koma inu mukuti, ‘Haa! Tingamuzunze bwanji,
29Inu muyenera kuopa lupanga;