1Yehova anandipatsa uthenga uwu kuti,
2“Iwe mwana wa munthu, Ine Ambuye Yehova ndikuwuza dziko la Israeli kuti:
3Chimaliziro chili pa iwe tsopano.
4Ine sindidzakumvera chisoni
5“Zimene ndikunena Ine Ambuye Yehova ndi izi:
6Chimaliziro chafika!
7Inu anthu okhala mʼdziko,
8Ine ndili pafupi kukukwiyirani,
9Ine sindidzakumvera chisoni
10“Taona, tsikulo!
11Chiwawa chasanduka ndodo
12Nthawi yafika!
13Wogulitsa sadzazipezanso zinthu
14“Lipenga lalira,
15Ku bwalo kuli kumenyana
16Onse amene adzapulumuka
17Dzanja lililonse lidzalefuka,
18Iwo adzavala ziguduli
19“Iwo adzataya siliva wawo mʼmisewu
20Iwo ankanyadira zodzikongoletsera zawo zamakaka
21Ndidzazipereka kwa alendo kuti azifunkhe.
22Ine ndidzawalekerera anthuwo
23“Konzani maunyolo,
24Ndidzabweretsa mitundu ya anthu oyipitsitsa
25Nkhawa ikadzawafikira
26Tsoka lidzatsatana ndi tsoka linzake,
27Mfumu idzalira,