We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Ezekieli 7

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Ezekieli 6 Ezekieli Ezekieli 8 →

1Yehova anandipatsa uthenga uwu kuti,

2“Iwe mwana wa munthu, Ine Ambuye Yehova ndikuwuza dziko la Israeli kuti:

3Chimaliziro chili pa iwe tsopano.

4Ine sindidzakumvera chisoni

5“Zimene ndikunena Ine Ambuye Yehova ndi izi:

6Chimaliziro chafika!

7Inu anthu okhala mʼdziko,

8Ine ndili pafupi kukukwiyirani,

9Ine sindidzakumvera chisoni

10“Taona, tsikulo!

11Chiwawa chasanduka ndodo

12Nthawi yafika!

13Wogulitsa sadzazipezanso zinthu

14“Lipenga lalira,

15Ku bwalo kuli kumenyana

16Onse amene adzapulumuka

17Dzanja lililonse lidzalefuka,

18Iwo adzavala ziguduli

19“Iwo adzataya siliva wawo mʼmisewu

20Iwo ankanyadira zodzikongoletsera zawo zamakaka

21Ndidzazipereka kwa alendo kuti azifunkhe.

22Ine ndidzawalekerera anthuwo

23“Konzani maunyolo,

24Ndidzabweretsa mitundu ya anthu oyipitsitsa

25Nkhawa ikadzawafikira

26Tsoka lidzatsatana ndi tsoka linzake,

27Mfumu idzalira,

← Ezekieli 6 Ezekieli Ezekieli 8 →