1“Imba nyimbo ya madandawulo, kuyimbira akalonga a ku Israeli.
2Uzinena kuti,
3Unalera mmodzi mwa ana ake,
4Anthu amitundu anamva za mkangowo,
5“ ‘Amayi aja ataona kuti mwana ankamukhulupirira uja wagwidwa ndi kuti chiyembekezo chake chapita padera,
6Unkayendayenda pakati pa mikango inzake,
7Unagwetsa malinga awo,
8Pamenepo mitundu ya anthu, makamaka ochokera madera ozungulira,
9Anawukoka ndi ngowe nawuponya mʼchitatanga.
10“ ‘Amayi ako anali ngati mpesa mʼmunda wamphesa
11Nthambi zake zinali zolimba,
12Koma unazulidwa mwaukali
13Ndipo tsopano anawuwokeranso ku chipululu,
14Moto unatulukanso mu mtengomo