We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Ezekieli 19

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Ezekieli 18 Ezekieli Ezekieli 20 →

1“Imba nyimbo ya madandawulo, kuyimbira akalonga a ku Israeli.

2Uzinena kuti,

3Unalera mmodzi mwa ana ake,

4Anthu amitundu anamva za mkangowo,

5“ ‘Amayi aja ataona kuti mwana ankamukhulupirira uja wagwidwa ndi kuti chiyembekezo chake chapita padera,

6Unkayendayenda pakati pa mikango inzake,

7Unagwetsa malinga awo,

8Pamenepo mitundu ya anthu, makamaka ochokera madera ozungulira,

9Anawukoka ndi ngowe nawuponya mʼchitatanga.

10“ ‘Amayi ako anali ngati mpesa mʼmunda wamphesa

11Nthambi zake zinali zolimba,

12Koma unazulidwa mwaukali

13Ndipo tsopano anawuwokeranso ku chipululu,

14Moto unatulukanso mu mtengomo

← Ezekieli 18 Ezekieli Ezekieli 20 →