We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Ezara 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Ezara 1 Ezara Ezara 3 →

1Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerako ku ukapolo, amene Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni anawagwira ukapolo ndi kupita nawo ku Babuloni (iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wake.

2Iwo anabwerera pamodzi ndi Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Seruya, Reelaya, Mordekai, Bilisani, Misipara, Bigivai, Rehumu ndi Baana).

3Zidzukulu za Parosi

4zidzukulu za Sefatiya

5zidzukulu za Ara

6zidzukulu za Pahati-Mowabu (zochokera kwa Yesuwa ndi Yowabu)

7zidzukulu za Elamu

8zidzukulu za Zatu

9zidzukulu za Zakai

10zidzukulu za Bani

11zidzukulu za Bebai

12zidzukulu za Azigadi

13zidzukulu za Adonikamu

14zidzukulu za Bigivai

15zidzukulu za Adini

16zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya)

17zidzukulu za Bezayi

18zidzukulu za Yora

19zidzukulu za Hasumu

20zidzukulu za Gibari

21Anthu a ku Betelehemu

22Anthu aamuna a ku Netofa

23Anthu aamuna a ku Anatoti

24Anthu aamuna a ku Azimaveti

25Anthu aamuna a ku Kiriati Yearimu, Kefira ndi Beeroti

26Anthu aamuna a ku Rama ndi Geba

27Anthu aamuna a ku Mikimasi

28Anthu aamuna a ku Beteli ndi Ai

29Anthu aamuna a ku Nebo

30Anthu aamuna a ku Magaibisi

31Anthu aamuna a ku Elamu wina

32Anthu aamuna a ku Harimu

33Anthu aamuna a ku Lodi, Hadidi ndi Ono

34Anthu aamuna a ku Yeriko

35Anthu aamuna a ku Sena

36Ansembe anali awa:

37Zidzukulu za Imeri

38Zidzukulu za Pasuri

39Zidzukulu za Harimu

40Alevi anali awa:

41Anthu oyimba nyimbo anali awa:

42Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa:

43Otumikira ku Nyumba ya Mulungu anali awa:

44zidzukulu za Kerosi, zidzukulu za Siyaha, Padoni,

45zidzukulu za Lebana, zidzukulu za Hagaba, zidzukulu za Akubu,

46zidzukulu za Hagabu, zidzukulu za Salimayi, zidzukulu za Hanani,

47zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari, zidzukulu za Reaya,

48zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nekoda, zidzukulu za Gazamu,

49zidzukulu za Uza, zidzukulu za Peseya, zidzukulu za Besai,

50zidzukulu za Asina, zidzukulu za Meunimu, Nefusimu,

51zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,

52zidzukulu za Baziruti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,

53zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema,

54zidzukulu za Neziya ndi zidzukulu za Hatifa.

55Zidzukulu za antchito a Solomoni zinali izi:

56zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,

57zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu,

58Chiwerengero cha onse otumikira ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za Solomoni chinali

59Anthu ali mʼmunsiwa anabwera kuchokera ku mizinda ya Teli-Mela, Teli-Harisa, Kerubi, Adoni ndi Imeri, ngakhale samatha kutsimikiza kuti mafuko awo analidi Aisraeli enieni kapena ayi:

60Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya, ndi zidzukulu za Nekoda. Onse pamodzi anali

61Ndi ena pakati pa ansembe anali awa:

62Amenewa anafufuza mayina awo mʼbuku lofotokoza mbiri ya mafuko awo, koma mayinawo sanawapezemo, choncho anawachotsa pa unsembe ngati anthu odetsedwa pa zachipembedzo.

63Bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo mpaka atapezeka wansembe wodziwa kuwombeza ndi Urimu ndi Tumimu.

64Chiwerengero cha anthu onse pamodzi chinali 42,360,

65kuwonjezera pamenepo, panalinso antchito awo aamuna ndi aakazi okwanira 7,337. Analinso ndi amuna ndi akazi oyimba nyimbo okwanira 200.

66Anali ndi akavalo 736, nyulu 245,

67ngamira 435 ndi abulu 6,720.

68Atafika ku Nyumba ya Yehova mu Yerusalemu, ena mwa atsogoleri a mabanja anapereka zopereka zaufulu zothandizira kumanganso Nyumba ya Mulungu pamalo pake pakale.

69Anapereka kwa msungichuma wa ntchitoyo molingana ndi mmene aliyense chuma chake chinalili: golide wa makilogalamu 500, siliva makilogalamu 2,800 ndi zovala za ansembe zokwanira 100.

70Ansembe, Alevi, oyimba nyimbo, alonda ndi antchito a ku Nyumba ya Yehova pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmidzi ya makolo awo.

← Ezara 1 Ezara Ezara 3 →