1Mbiri yabwino ndi yopambana mafuta onunkhira bwino,
2Kuli bwino kupita ku nyumba yamaliro
3Chisoni nʼchabwino kusiyana ndi kuseka,
4Mtima wa munthu wanzeru nthawi zonse umalingalira za imfa,
5Kuli bwino kumva kudzudzula kwa munthu wanzeru
6Kuseka kwa zitsiru kuli ngati
7Kuzunza ena kumasandutsa munthu wanzeru kukhala chitsiru,
8Mathero ake a chinthu ndi abwino kupambana chiyambi chake,
9Usamafulumire kukwiya mu mtima mwako,
10Usamafunse kuti, “Nʼchifukwa chiyani masiku amakedzana anali abwino kupambana masiku ano?”
11Nzeru ngati cholowa, ndi chinthu chabwino
12Nzeru ndi chitetezo,
13Taganizirani zimene Mulungu wazichita:
14Pamene zinthu zili bwino, sangalala;
15Pa moyo wanga wopanda phinduwu ndaona zinthu ziwiri izi:
16Usakhale wolungama kwambiri
17Usakhale woyipa kwambiri,
18Nʼkwabwino kuti utsate njira imodzi,
19Nzeru zimapereka mphamvu zambiri kwa munthu wanzeru
20Palibe munthu wolungama pa dziko lapansi
21Usamamvetsere mawu onse amene anthu amayankhula,
22pakuti iwe ukudziwa mu mtima mwako
23Zonsezi ndinaziyesa ndi nzeru zanga ndipo ndinati,
24Nzeru zimene zilipo,
25Kotero ndinayikapo mtima wanga kuti ndidziwe,
26Ndinapeza kanthu kowawa kupambana imfa,
27Mlaliki akunena kuti, “Taonani, chimene ndinachipeza ndi ichi:
28pamene ine ndinali kufufuzabe
29Chokhacho chimene ndinachipeza ndi ichi: