We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

2 Samueli 22

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← 2 Samueli 21 2 Samueli 2 Samueli 23 →

1Davide anayimbira Yehova nyimbo iyi pamene Yehovayo anamupulumutsa mʼdzanja la adani ake onse ndiponso mʼdzanja la Sauli.

2Iye anati,

3Mulungu wanga ndiye thanthwe langa, mʼmene ndimathawiramo,

4“Ndimayitana Yehova amene ndi woyenera matamando,

5“Mafunde a imfa anandizinga;

6Anandimanga ndi zingwe za ku manda;

7“Mʼmasautso anga ndinapemphera kwa Yehova;

8“Dziko lapansi linanjenjemera ndi kuchita chivomerezi,

9Mʼmphuno mwake munatuluka utsi;

10Iye anangʼamba thambo natsika pansi;

11Iye anakwera pa Kerubi ndi kuwuluka;

12Iye anapanga mdima kukhala chofunda chake,

13Mʼkuwala kumene kunali pamaso pake

14Yehova anabangula kumwamba ngati bingu,

15Iye anaponya mivi yake, nabalalitsa adani ake,

16Zigwa za mʼnyanja zinaonekera poyera,

17“Ali kumwamba, Iye anatambalitsa dzanja lake ndipo anandigwira;

18Anandipulumutsa kwa mdani wanga wamphamvu,

19Adaniwo analimbana nane pamene ndinali pa mavuto,

20Iye anandipititsa kumalo otakasuka;

21“Yehova wandithandiza molingana ndi chilungamo changa;

22Pakuti ine ndinatsata njira za Yehova;

23Malamulo ake onse ali pamaso panga,

24Ndakhala moyo wosalakwa pamaso pake

25Yehova wandipatsa mphotho molingana ndi chilungamo changa,

26“Kwa wokhulupirika, Inu mumaonetsa kukhulupirika kwanu,

27Kwa woyera mtima, Inu mumaonetsa kuyera mtima kwanu,

28Inu mumapulumutsa anthu odzichepetsa,

29Inu Yehova, ndinu nyale yanga;

30Ndi thandizo lanu nditha kulimbana ndi gulu la ankhondo,

31“Kunena za Mulungu, zochita zake ndi zangwiro;

32Mulungu wina ndi uti wofanana nanu Yehova?

33Ndi Mulungu amene anandipatsa mphamvu

34Iye amasandutsa mapazi anga kukhala ngati ambawala yayikazi;

35Iye amaphunzitsa manja anga kuchita nkhondo;

36Inu mundipatsa ine chishango chanu cha chigonjetso;

37Inu mwalimbitsa njira yanga kuti ndiyende bwino,

38“Ine ndinathamangitsa adani anga ndi kuwakantha;

39Ndinawakantha kotheratu, ndipo sanathe kudzukanso;

40Inu munandipatsa ine mphamvu yochitira nkhondo;

41Inu muchititsa kuti adani anga atembenuke ndi kuthawa;

42Iwo anafuwula kupempha thandizo, koma panalibe ndi mmodzi yemwe owapulumutsa.

43Ine ndinawaperesa ngati fumbi la pa dziko lapansi;

44“Inu mwandipulumutsa mʼmanja mwa mitundu ya anthu;

45Alendo amadzipereka okha pamaso panga;

46Iwo onse anataya mtima;

47“Yehova ndi wamoyo! Litamandidwe Thanthwe langa.

48Iye ndi Mulungu amene amabwezera chilango,

49amene amandimasula mʼmanja mwa adani anga.

50Choncho ine ndidzakutamandani Inu Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina;

51“Iye amapereka chipambano chachikulu kwa mfumu yake,

← 2 Samueli 21 2 Samueli 2 Samueli 23 →